Tuesday, December 9, 2008

Onyamata

Ine ndine Alick Kadango Bwanali, mnyamata wa ko Mbuna ku Mpenu ko Mazengera.
Ine ndimakonda kucheza ndi kuseka kwambiri. Choncho tsamba lino ndi bwalo la nseketso komanso pa majiga podziwitsirana zochitika pakati pathu. Ndimakonda kuyenda ndikuona malo osiyanasiyana, kuwerenga komanso kuwonera kuti ndizidziwa zomwe zikuchitika kunjaku. Ndikukhulupirira kuti ticheza pabwaloli!

Onyamata AKB

No comments: